Ndikupita ku Africa kuona abale wanga.
(I’m going to Africa to see my people!)
Christmas ya bwino!
(Merry Christmas)
x
*insert high-pitched scream here* Ndapeza M’malawi pa Tumblr! Ayi, I’m beyond ecstatic. Koma ndili jelasi kuti ukupita ku Malawi, ine mwina mu Juni ya chaka cha mawa :(.